Kbg - Zoononga Moyo Lyrics

  • Artist/Band:
  • Album:
  • Song Title:
  • Text Options:
  • Share & Like:

Verse 1:LAWI
Amati bawa
ndi njira yochotsela nkhawa
nanga bwanji ukadzuka mmawa
matsile maluzi uliso confused
ndingonena chindunji
chenicheni nchiti
chokhalila mfiti
when in actual sense you r a slave to the sin that yo glue to
iwe tchimo litavala umunthu
chonde ndithandizeni
ndidziweko swaga as much as i know ndizoononga moyo wanga
sikuzikweza kodi?
Kuwalila kodi?
Kukhutitsidwa ndimmene ndavalila kodi?
Inde asungwana apapa mukukhwana titha kuyamikila mpakana kupanga mwana

Inde abwana mwatchena osanama but check on the . . . Ndiyesu mwasemphana
u can be who u want to b
multiply zinthu ngati tyms
u can buy evrything with paper
but heaven uuuh uuuh zachisoni pepa

{Chorus:}
kodi wapindulanji iweyo
utapeza zonse zofuna mtima wako
koma zonse zomwe wapezazo
mulibe chipulumutso
ndizinthu zoonona moyo wako x2

Verse2:KBG
lawi nane ndiwauze fanzi
. . . .

Search Song Lyrics
Browse Artists

A B C D E F G H I J K L M N
O P Q R S T U V W X Y Z #

Hide preview
Lyrics and Video Widget:

Code for your site/blog/space

Click above to select the code then right click & copy to get the code to paste onto your site/blog